24
Dec 2018

MBEWU ZACHIPAMBANO – Lolemba, 24 December, 2018 Chisankho n’chanu kukhala moyo wochita bwino Ndi M’tumwi Joseph Ziba Buku ili la chilamulo lisachoke pakamwa pako; koma ulingiriremo usana ndi usiku, kuti usamalire kuchita monga mwa zonse zolembedwamo; popeza ukatero udzakometsa njira yako, nudzachita mwanzeru. Yoswa 1: 8 KJV Tsiku lina, posinkhasinkha ndi kullingalira Mawu a Mulungu, Atate adanditsegula maso ku mfundo zomwe zimapangitsa munthu kupambana mwaumulungu m’moyo uno. Pamene ndinkangokhalira kukondwera ndikudziviika mu zomwe Atate amavumbulutsa, Iye anandifusa funso lomwe limaoneka ngati “losamvetsetseka.’ Iye anati: “Mwana wanga, Kodi umaganiza kuti n’chifukwa chiyani ndidayikiza mfundo zokhudzana ndi......
Read More
October 29, 2018
Know What Works for You – Apostle Joseph Ziba
SEEDS OF VICTORY – 29th October 2018 Know What Works for You – Apostle Joseph Ziba “And Saul’s servants spake those words in the ears of David. And David said, Seemeth it to you a light thing...
April 27, 2018
Why Rising on Top?
WHY RISING ON TOP Some people have been asking me why we call these meetings “Rising On Top” instead of “Rising to the Top”. They feel like naming these meetings “Rising to the Top”...